album cover
Anthu
album cover
Anthu fue lanzado el 13 de noviembre de 2025 por 7433591 Records DK como parte del álbum CHOSEN
ÁlbumCHOSEN
13 de noviembre de 2025
Sello discográfico7433591 Records DK
IdiomaEnglish
BPM100
Melodía
Nivel de sonidos acústicos
Valence
Capacidad para bailar
Energía

Letra

Jagga
Mmh Jagga
Prince mmh Jagga
Zatheka bwa
Kuswela mtima dolo ngati ine zomwe ndili nazo
Zavuta bwa
Ndaziwano kuti siiona nkhope heartbreak
Ndachilapa
Kuswela mtima dolo ngati ine zomwe ndili nazo
Zavuta bwa
Ndaziwano kuti siiona nkhope heartbreak
M'mene ndakongolela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
M'mene ndimatchenela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
For sure for sure
Mpaka kuswela mtima msilikali ati akuombele iwe
For sure for sure
Mpaka kuswela mtima chigigo simuopa Kupondedwa
Mbili munaononga kale anthu oyipa inuyo
Zoti ndiwa asthma simuona
Olo zoti kwathu munafika kale sizikukhuzani inuyo
No feeling pity inuyo
Mulibe mantha inuyo
Wamasiye kale ine
( kundisiya choncho)
Wama dimples ine
( mpaka kundisiya choncho)
Duntuntu ine
Hmm waaa khunyu ine
( mpaka kundisiya choncho)
M'mene ndakongolela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
M'mene ndimatchenela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
Mpaka kuswela mtima doctor
Kunamiza wa polisi mpaka ku gonja
Politician wandaleyu sakuopsani
Kuwatchita abusa azaku otchani
Ambuye akuoneni
Kusiya mfana opusha hustle ( waluza ndiwe)
Kundisiya poti ndima Beta ( waluza)
Kasiye mfana oyendela paso ( waluza ndiwe)
Kusiya mfana ogeza ( waluza)
Wamasiye kale ine
( kundisiya choncho)
Wama dimples ine
( mpaka kundisiya choncho)
Duntuntu ine
Hmm waaa khunyu ine
( mpaka kundisiya choncho)
M'mene ndakongolela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
M'mene ndimatchenela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
Written by: Chawanagwa Ngoma, Mwabi Prince Chitedze
instagramSharePathic_arrow_out􀆄 copy􀐅􀋲

Loading...