album cover
Anthu
33
Afro-Beat
Anthu è stato pubblicato il 13 novembre 2025 da 7433591 Records DK come parte dell'album CHOSEN
album cover
AlbumCHOSEN
Data di uscita13 novembre 2025
Etichetta7433591 Records DK
Melodicità
Acousticità
Valence
Ballabilità
Energia
BPM100

Crediti

COMPOSITION & LYRICS
Prince chitz
Prince chitz
Songwriter
Chawanagwa Ngoma
Chawanagwa Ngoma
Songwriter
PRODUCTION & ENGINEERING
Chawabeats
Chawabeats
Producer

Testi

Jagga
Mmh Jagga
Prince mmh Jagga
Zatheka bwa
Kuswela mtima dolo ngati ine zomwe ndili nazo
Zavuta bwa
Ndaziwano kuti siiona nkhope heartbreak
Ndachilapa
Kuswela mtima dolo ngati ine zomwe ndili nazo
Zavuta bwa
Ndaziwano kuti siiona nkhope heartbreak
M'mene ndakongolela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
M'mene ndimatchenela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
For sure for sure
Mpaka kuswela mtima msilikali ati akuombele iwe
For sure for sure
Mpaka kuswela mtima chigigo simuopa Kupondedwa
Mbili munaononga kale anthu oyipa inuyo
Zoti ndiwa asthma simuona
Olo zoti kwathu munafika kale sizikukhuzani inuyo
No feeling pity inuyo
Mulibe mantha inuyo
Wamasiye kale ine
( kundisiya choncho)
Wama dimples ine
( mpaka kundisiya choncho)
Duntuntu ine
Hmm waaa khunyu ine
( mpaka kundisiya choncho)
M'mene ndakongolela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
M'mene ndimatchenela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
Mpaka kuswela mtima doctor
Kunamiza wa polisi mpaka ku gonja
Politician wandaleyu sakuopsani
Kuwatchita abusa azaku otchani
Ambuye akuoneni
Kusiya mfana opusha hustle ( waluza ndiwe)
Kundisiya poti ndima Beta ( waluza)
Kasiye mfana oyendela paso ( waluza ndiwe)
Kusiya mfana ogeza ( waluza)
Wamasiye kale ine
( kundisiya choncho)
Wama dimples ine
( mpaka kundisiya choncho)
Duntuntu ine
Hmm waaa khunyu ine
( mpaka kundisiya choncho)
M'mene ndakongolela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
M'mene ndimatchenela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
Written by: Chawanagwa Ngoma, Mwabi Prince Chitedze
instagramSharePathic_arrow_out􀆄 copy􀐅􀋲

Loading...