album cover
Mabala
658
Reggae
Mabala è stato pubblicato il 29 ottobre 2012 da Malawi Goodlife come parte dell'album Son of the Poor Man
album cover
Data di uscita29 ottobre 2012
EtichettaMalawi Goodlife
Melodicità
Acousticità
Valence
Ballabilità
Energia
BPM160

Crediti

PERFORMING ARTISTS
Lucius Banda
Lucius Banda
Performer
COMPOSITION & LYRICS
Lucius Banda
Lucius Banda
Composer

Testi

Panali anthu ena wongovutika
Pamene anthu ena amkangokondwera
Panalia anthu ena wogwira ntchito
Pamene anthu ena amkangodyelera
Malume ndalama kubisa ku bank
Pamene mbumba yanu ikufa ndi njala
Koma zowuluka zonse zitawuluka
Pali tsiku limodzi zitadzatele
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Analanda ufumu kalero
Nawupeleka kwa woyenera
Ndichani chingamulake
Mbuye Mulungu wachilungamo!
Ndi wachikondi
Tsiku la Mulungu ndi lopambana
Koma linali tsiku la masewera
Amayi kulephera kusunga banja
Koma Ambuye sanakondwere nazo
Anthu anzeru opempha chilungamo
Amkangofa monga muja zifera ntchetche
Koma zowuluka zonse zitawuluka
Pali tsiku limodzi zitadzatele
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Analanda ufumu kalero
Nawupeleka kwa woyenera
Ndichani chingamulake
Mbuye Mulungu wachilungamo!
Ndi wachikondi
Ukhululuke iwe nzanga ofedwa
Puputa misozi tiyiwale zonse
Nyali yawala nkhuku ija yathawa
Tisangalare poti Mbuye watikumbuka
Zokulipa diso izo siyani
Zikanatero bwezi tonse tili a khungu
Kukhululuka ndiye ndakhululuka
Koma mabalawa ndiye akupweteka
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Analanda ufumu kalero
Nawupeleka kwa woyenera
Ndichani chingamulake
Mbuye Mulungu wachilungamo!
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Analanda ufumu kalero
Nawupeleka kwa woyenera
Ndichani chingamulake
Mbuye Mulungu wachilungamo!
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Analanda ufumu kalero
Nawupeleka kwa woyenera
Ndichani chingamulake
Mbuye Mulungu wachilungamo!
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Written by: Lucius Banda
instagramSharePathic_arrow_out􀆄 copy􀐅􀋲

Loading...