Lyrics

M'ma Makadidido eeh Oh yeah, oh yeah, ooh yeah I know it's not okay Kuti nthawi zonse nzikukulonda iwe Baby I can't help it I still believe the odds will play in my favour Do you think of me? Olo mwina zoti ndakusowa iweyo Nthawi yonseyi Ndinkaganiza zoti sungagwidwe Kapena mwina m'minyama ah Zoti unandithawa ah Pano yatsala ndi nkhawa ah Iwe sunkandikonda ah Kodi unandinamiza? ah When you told me love always wins Ine ndimanva kuwawa Daily nkama ku stalker ah I know it's not okay It's not okay It's not okay It's not okay Baby I am desperate I am desperate I am desperate I am desperate Ma ine, ma ine Daily m'mangoganiza za iwe Anzanga nawo amathoka za iwe Anzako nawo akuti you're happy iwe Nnaziyambilanji za chikondi izi? Zanga zimangothela misonzi Why do you look better and excited? Zaka zonsezi sunawonekepo chonchi iwe Kapena mwina m'minyama ah Zoti unandithawa ah Pano yatsala ndi nkhawa ah Iwe sunkandikonda ah Kodi unandinamiza? ah When you told me love always wins Ine ndimanva kuwawa Daily nkama ku stalker and I know it's not okay It's not okay It's not okay It's not okay Baby I am desperate I am desperate I am desperate I am desperate Kapena mwina m'minyama ah Zoti unandithawa ah Pano yatsala ndi nkhawa ah Iwe sunkandikonda ah Kodi unandinamiza? ah When you told me love always wins Ine ndimanva kuwawa Daily nkama ku stalker ah
Writer(s): Teddy Maliza Lyrics powered by www.musixmatch.com
instagramSharePathic_arrow_out