Lyrics

Woooo Hahaha Sisonke neh Lero nde tiuchapatu eeeh Iwe Wani Sauzande yonseyo ndimwere mowa ine Mphwanga maluzi samakuchapa dollar yonseyo ndingabande Mwezi wachikhalire Bhola M'mene ikutchipila mu bangwe Kwa hiki kwa chichi Rasta Mellz Kumpanje Ma husha Sha sha alabwe ma husha Tidya koma mochedwa hah Tidyera ngosha lero sitikulora bona ma Sosha Mabebeza kundipeza akufuna ma Sosha Timweseni castle Ngati Ali Fili handede Tenga Dollar sitikutola tikuvuulira mchenga Nip imodzi ujibe nawo aah iwe tchenga tchenga Olo zindipweteka ine ndilipira ndekha Ulibe money Eti Wabwera dala cholinga tizikangana Eti Botolo mwan'nyamula?mulibe kanthu Eti Tiziti ndinu mabwana mwagwera mu fridge tchubu Eti Kudabwa mwa'nlubwa Biggy tengani hunters uyu Aaah iwe fanta chani Ganja palibetu apa Aaah iwe chamba chani Kwabwera ma husha Nde ukuwasiya panja Abwere alowe chifukwa Tikufuna zipweteko Pweteko pweteko pweteko zipweteko Pweteko pweteko Tikufuna zipweteko Pweteko pweteko pweteko Zipweteko Pweteko pweteko pweteko Yomweyo galu iweeee
Writer(s): Mellanie Msumba Lyrics powered by www.musixmatch.com
instagramSharePathic_arrow_out