album cover
Anthu
26
Afro-Pop
Anthu was released on November 13, 2025 by 7433591 Records DK as a part of the album CHOSEN
album cover
AlbumCHOSEN
Release DateNovember 13, 2025
Label7433591 Records DK
Melodicness
Acousticness
Valence
Danceability
Energy
BPM100

Credits

COMPOSITION & LYRICS
Prince chitz
Prince chitz
Songwriter
Chawanagwa Ngoma
Chawanagwa Ngoma
Songwriter
PRODUCTION & ENGINEERING
Chawabeats
Chawabeats
Producer

Lyrics

Jagga
Mmh Jagga
Prince mmh Jagga
Zatheka bwa
Kuswela mtima dolo ngati ine zomwe ndili nazo
Zavuta bwa
Ndaziwano kuti siiona nkhope heartbreak
Ndachilapa
Kuswela mtima dolo ngati ine zomwe ndili nazo
Zavuta bwa
Ndaziwano kuti siiona nkhope heartbreak
M'mene ndakongolela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
M'mene ndimatchenela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
For sure for sure
Mpaka kuswela mtima msilikali ati akuombele iwe
For sure for sure
Mpaka kuswela mtima chigigo simuopa Kupondedwa
Mbili munaononga kale anthu oyipa inuyo
Zoti ndiwa asthma simuona
Olo zoti kwathu munafika kale sizikukhuzani inuyo
No feeling pity inuyo
Mulibe mantha inuyo
Wamasiye kale ine
( kundisiya choncho)
Wama dimples ine
( mpaka kundisiya choncho)
Duntuntu ine
Hmm waaa khunyu ine
( mpaka kundisiya choncho)
M'mene ndakongolela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
M'mene ndimatchenela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
Mpaka kuswela mtima doctor
Kunamiza wa polisi mpaka ku gonja
Politician wandaleyu sakuopsani
Kuwatchita abusa azaku otchani
Ambuye akuoneni
Kusiya mfana opusha hustle ( waluza ndiwe)
Kundisiya poti ndima Beta ( waluza)
Kasiye mfana oyendela paso ( waluza ndiwe)
Kusiya mfana ogeza ( waluza)
Wamasiye kale ine
( kundisiya choncho)
Wama dimples ine
( mpaka kundisiya choncho)
Duntuntu ine
Hmm waaa khunyu ine
( mpaka kundisiya choncho)
M'mene ndakongolela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
M'mene ndimatchenela inemu
( anthu mulibe chisoni)
Zoona kundiswela mtima ine koma hmm mmh
Anthu ndioyipa awa
Written by: Chawanagwa Ngoma, Mwabi Prince Chitedze
instagramSharePathic_arrow_out􀆄 copy􀐅􀋲

Loading...