album cover
Msamatero
155
Reggae
Msamatero was released on October 29, 2012 by Malawi Goodlife as a part of the album Yahwe
album cover
AlbumYahwe
Release DateOctober 29, 2012
LabelMalawi Goodlife
Melodicness
Acousticness
Valence
Danceability
Energy
BPM123

Music Video

Music Video

Credits

PERFORMING ARTISTS
Lucius Banda
Lucius Banda
Performer
COMPOSITION & LYRICS
Lucius Banda
Lucius Banda
Composer

Lyrics

Iya-ya-ya, ya-ya lero
Iya-ya-ya, ya-ya lero
Iya-ya-ya, ya-ya lero
Iya-ya-ya, ya-ya lero
Achimwene mukundiwopsa, oh
Vuto lanu ndi chiyani, oh
Kuti muyiwale nthawi yomweyi, oh
Kumudzi m'dasiya kubwera
Ati galimoto singafika
Kufuna nzamvere na mame, oh
Kuti bambo anu amwalira
Bambo anu afa ndi njala
Achimwene msamatero anzanu akulira
Makolo anapita, anu muwanyoza
Anzanu akudandawula, amayi wanga akanakhala moyo nkanawasamala
Iya-ya-ya, ya-ya lero
Iya-ya-ya, ya-ya lero
Ayi-ya-ya, ya-ya lero
Iya-ya-ya, ya-ya lero
Galimoto wasongola
Cellular yako kolekele
Bambo ako akuvutika, oh
Anadumula ovololo
Kupanga jekete ndi buluku, oh
Kuwujika zomanga nyumba, oh
Aphwako ayitanira ma bus, oh
Katundu yense adagulitsa uphunzire
Achimwene msamatero anzanu akulira
Makolo anapita, anu mukuwanyoza
Anzanu akudandawula, amayi wanga akanakhala moyo nkanawasamala
Iya-ya-ya, ya-ya lero
Iya-ya-ya, ya-ya lero
Iya-ya-ya, ya-ya lero
Wathewera
Iya-ya-ya, ya-ya lero
Iya-ya-ya, ya-ya lero
Achimwene msamatero anzanu akulira
Makolo adapita, anu mukuwanyoza
Anzanu akudandawula, amayi wanga akanakhala moyo nkanawasamala
Written by: Lucius Banda
instagramSharePathic_arrow_out􀆄 copy􀐅􀋲

Loading...