album cover
Pray Hard, Work Hard
165
Christian & Gospel
Pray Hard, Work Hard was released on May 29, 2026 by Lopa kulture as a part of the album God Is Present
album cover
Release DateMay 29, 2026
LabelLopa kulture
LanguageEnglish
Melodicness
Acousticness
Valence
Danceability
Energy
BPM90

Music Video

Music Video

Credits

PERFORMING ARTISTS
Lopa kulture
Lopa kulture
Drums
COMPOSITION & LYRICS
Sampa Lopa
Sampa Lopa
Songwriter
PRODUCTION & ENGINEERING
Lopa kulture
Lopa kulture
Executive Producer

Lyrics

Yahweh…
Yahweh…
Eeh…
Chikhulupiriro chopanda ntchito…
ni chakufa…
Eeh...
Eeh...
Chikhulupiriro chopanda ntchito…
ni chakufa…
Amaona Madalitso koma sadziwa mbiri
Even through hard times I chased glory
Ndimapemphera kwa Mulungu tsiku ndi tsiku
Koma ndimagwiranso ntchito osangokhala mblu
Olo zinandivuta bwangi sindinataye chiyembekezo
Noah anapemphera koma anamanga chombo
David anakhulupirira koma anamenyanso nkhondo
Peter anakhulupirira koma anaponya neti...
Faith without works is dead
Mulungu amatsegula chiseko koma uyenera kuyenda ndikupita
Madalitso awa mukuona....
Ndinawapempherera...
Ndinawagwirira ntchito...
I gave my all.... ( My all)
And left the rest in the hands of God....
And He came through bigger than I imagined...
I prayed hard... (in faith)
Worked hard... (in strength)
Now Jehovah opened doors
Nobody can close… (Never)
Ninasunga chikulupiriro kosatopa...
Ninapitiriza osaleka... (osaleka)
Tsopano kumwamba kwandidalitsa
Chifukwa cha ntchito yanga
Mulungu anadalitsa Ntchito ya manja anga
When God says yes...
Nobody can say no... (Awe Awe)
Not even the devil... (no)
Not the haters... (no)
Not the fear of failures... (No)
Every seed that I planted in pain... (Amen)
Now returning back with gain... (Amen)
I was tired but I never quit... ( praise God)
Now my testimony makes sense... (testimony)
Some people keep waiting for a miracle
While wasting time being comfortable
God gives vision, not excuses...
Blessings come when purpose moves you
Moses still had to lift the rod
Before the sea was opened by God
So every day I woke up fighting
Trusted heaven while I kept grinding
Kneeling in prayer then standing tall
Trusting God through every fall... (yes)
These blessings you see... (yes)
I prayed for them... (yes)
I sweated for them... (yes)
I prayed… (truly)
I did my part
And God did the impossible...
Now my life becoming undeniable...
I prayed hard... (in faith)
Worked hard... (in strength)
Now Jehovah opened doors
Nobody can close… (Never)
Ninasunga chikulupiriro kosatopa...
Ninapitiriza osaleka... (osaleka)
Tsopano kumwamba kwandidalitsa
Chifukwa cha ntchito yanga
Mulungu anadalitsa Ntchito ya manja anga
When God says yes...
Nobody can say no... (Awe Awe)
Not even the devil... (no)
Not the haters... (no)
Not the fear of failures... (No)
I was planting through the tears
Now I’m harvesting for years
God was watching every sacrifice
Every sleepless night I had to face
I trusted God with all my soul
But still worked hard to reach my goal
Now the blessings overflowing
Favor on me fully showing
Pray…
trust God…
Pray…
trust God…
Pray...
Trust God...
Pray...
I prayed hard... (in faith)
Worked hard... (in strength)
Now Jehovah opened doors
Nobody can close… (Never)
Ninasunga chikulupiriro kosatopa...
Ninapitiriza osaleka... (osaleka)
Tsopano kumwamba kwandidalitsa
Chifukwa cha ntchito yanga
Mulungu anadalitsa Ntchito ya manja anga
When God says yes...
Nobody can say no... (Awe Awe)
Not even the devil... (no)
Not the haters... (no)
Not the fear of failures... (No)
Ndinapemphera…
Ndinagwira ntchito…
Yehova anandichitira zazikulu
Kuposa momwe ndimaganizira…
Amen… (Amen)
Amen... (Amen)
Written by: Sampa Lopa
instagramSharePathic_arrow_out􀆄 copy􀐅􀋲

Loading...