album cover
Mabala
660
Reggae
Mabala adlı parça albümünün bir parçası olarak Malawi Goodlife tarafından 29 Ekim 2012 tarihinde yayınlandıSon of the Poor Man
album cover
Çıkış Tarihi29 Ekim 2012
FirmaMalawi Goodlife
Melodiklik
Akustiklik
Valence
Dans Edilebilirlik
Enerji
BPM160

Krediler

PERFORMING ARTISTS
Lucius Banda
Lucius Banda
Performer
COMPOSITION & LYRICS
Lucius Banda
Lucius Banda
Composer

Şarkı sözleri

Panali anthu ena wongovutika
Pamene anthu ena amkangokondwera
Panalia anthu ena wogwira ntchito
Pamene anthu ena amkangodyelera
Malume ndalama kubisa ku bank
Pamene mbumba yanu ikufa ndi njala
Koma zowuluka zonse zitawuluka
Pali tsiku limodzi zitadzatele
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Analanda ufumu kalero
Nawupeleka kwa woyenera
Ndichani chingamulake
Mbuye Mulungu wachilungamo!
Ndi wachikondi
Tsiku la Mulungu ndi lopambana
Koma linali tsiku la masewera
Amayi kulephera kusunga banja
Koma Ambuye sanakondwere nazo
Anthu anzeru opempha chilungamo
Amkangofa monga muja zifera ntchetche
Koma zowuluka zonse zitawuluka
Pali tsiku limodzi zitadzatele
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Analanda ufumu kalero
Nawupeleka kwa woyenera
Ndichani chingamulake
Mbuye Mulungu wachilungamo!
Ndi wachikondi
Ukhululuke iwe nzanga ofedwa
Puputa misozi tiyiwale zonse
Nyali yawala nkhuku ija yathawa
Tisangalare poti Mbuye watikumbuka
Zokulipa diso izo siyani
Zikanatero bwezi tonse tili a khungu
Kukhululuka ndiye ndakhululuka
Koma mabalawa ndiye akupweteka
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Analanda ufumu kalero
Nawupeleka kwa woyenera
Ndichani chingamulake
Mbuye Mulungu wachilungamo!
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Analanda ufumu kalero
Nawupeleka kwa woyenera
Ndichani chingamulake
Mbuye Mulungu wachilungamo!
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Analanda ufumu kalero
Nawupeleka kwa woyenera
Ndichani chingamulake
Mbuye Mulungu wachilungamo!
Inu mumati zidzakhala choncho
Mpaka liti abale?
Ana a Mulungu sangakhale akulira
Masiku onse a moyo wawo
Written by: Lucius Banda
instagramSharePathic_arrow_out􀆄 copy􀐅􀋲

Loading...